Watch and Download Music Video



Download this video

Vote For This Song

Lyrics

Kumbire adanka nawo /

Palibe akanakhonza /

Anasiya pa dzuwa anawo

/ Anayesa ndi malodza /Ankati satana

/ Wakhala pa nsana / Kuyamba kudana

/ Kufuna kuphana Kuthana /

Nzosauzana /

Nthawi yakwana /

Buluzi wa easy chitseko cha mpana

CHORUS

Anapita ndi nyanga zomwe kumanda / Anapita ndi nyanga zomwe kumanda /

Ayo Tsoka Liyenda / Ayo Tsoka Liyenda

Bambo awa anali chikhwaya /

Ana moyo wawo sanamve kuwawa / Ku school akapita amathawa / Zinavuta ndi za nchere analawa / Yes Sanauzidwe za moyo / Anapeza bwanji makolo/Chuma/Moyo unakoma/Opanda zo khoma/Kupeza izo afuna/Ohh dzi ana ulesi/Bambo awo atsamira nkono

Akuti zonsezi /Ndi curse/Chayabwa chitedze/Mavuto pang'ono see they stressed/

CHORUS

Mudziwaphunzitsa ana/SiKupangira pa mawa/Asamayese ngati ophweka moyo/Mukadzapita adzakhala akapolo/ Musama yiwale/Kuti zanu munapanga kale/Nzeru zanu sizingatsale/Mungadzavutitse abale/Mdzakolola zomwe mudzale/Chuma ichi sangasamale/Ngati panopa simuphunzitsa/Mapangidwe ake mukumpusitsa/Tsoka ilo

CHORUS


Songwriters

Piksy

Sharing is cool

You may also like...



Mobile Site

To view this page on the Malawi-Music.com mobile site Click here

Review

Piksy is back! New single, and new album on the way.

Comments
Hits 67001 Plays. | 84875 Downloads.

Follow Malawi Music on Instagram