Vote For This Song

Lyrics

Bebie upitirize

Intro:

Ndi Alinafe e! Jimu bebie ndikuti upitireze, upitireze kundikonda.

VERSE ONE

Tachoka kutali iwe, tapanga chibwenzi mokwanira 
Tazemeberana bebie. Sono lero ndikufuna kuti,
Tingomanga oyera, aliyense adziwe. 
Kuyambira pa chibwezi, sinaone vutto lina lililonse kwaa iwe,
Chako chinali chikondi. Koma poti achikondi ambiri,
Amayamba bwino chonchi, koma sapitiriza.
Ndichifukwa chake ngakhale chikondi sapempha,
Ndikupempha upitirize, usalekelere panjira bebie.
Bebie! Bebie!

Chorus

Bebie upitirize x2
Upitirize kundikonda.
Sweet upitirize, ladie upitirize! Upitirize kundikonda.
Bebiee! X2 upitirize kundikonda.

VERSE TWO

Analiponso wena dzana, anayamba ndichikondi koma sanapitirize.
Ambiri amango kondana pachi bwenzi pokha, kumamasukirana kumayenda shosholo,
Akakwtirana mumv agawanapo zida.
Pamene tikugwirizana dziwa alipo ena, ofuna tidane azitiseka, 
Chonde usawapatse m’pata.
Zomwe nkuchita m’paka mubanja ndzaona chikondi changa
Sichidzasintha. Bebie! X2

Chorus


Songwriters

Alinafe Jimu

Sharing is cool

You may also like...



Mobile Site

To view this page on the Malawi-Music.com mobile site Click here

Review

Comments
Hits 5165 Plays. | 1743 Downloads.
« Mabanja Aphweka aka Zinyenyeswa Time is money (Live Acoustic) Songs Wamoyo Sayamikidwa ft Duster Namakhwa »

Follow Malawi Music on Instagram